Ubuntu amabwela ndi Firefox, bulawuza yomwe anthu zikwi amagwilitsa ntchito dziko lonse lapansi. Komanso mapologalamu ena omwe mungathe kugwilitsa ntchito zapa intaneti pafupi pafupi (monga Facebook kapena Gmail, mwa chitsanzo) mutha ku dinda kapena kutsindikiza pa mwamba pa komputa yanu kuti mudzigwilitsa ntchito mwachangu, monga zikhalila ndi mapologalamu ena mukomputa mwanu.
Mapologalamu oyendetsela komputa amwe awonjezeledzwa.
-
Firefox pulauza wa intaneti
Ma Software amwe alindi chithandizo
-
Chromium